Masalimo 102:26 - Buku Lopatulika26 Zidzatha izi, koma Inu mukhala: Inde, zidzatha zonse ngati chovala; mudzazisintha ngati malaya, ndipo zidzasinthika: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Zidzatha izi, koma Inu mukhala: Inde, zidzatha zonse ngati chovala; mudzazisintha ngati malaya, ndipo zidzasinthika: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Zonsezi zidzatha ngati malaya, koma Inu mulipobe. Inu mumazisintha ngati chovala, ndipo zimatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Izi zidzatha, koma Inu mudzakhalapo; zidzatha ngati chovala. Mudzazisintha ngati chovala ndipo zidzatayidwa. Onani mutuwo |