Masalimo 102:24 - Buku Lopatulika24 Ndinati, Mulungu wanga, musandichotse pakati pa masiku anga: Zaka zanu zikhalira m'mibadwomibadwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndinati, Mulungu wanga, musandichotse pakati pa masiku anga: Zaka zanu zikhalira m'mibadwomibadwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Ndikuti, “Mulungu wanga, musandichotse tsopano ndisanakalambe, Inu amene zaka zanu sizitha mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Choncho Ine ndinati: “Musandichotse, Inu Mulungu wanga, pakati pa masiku a moyo wanga; zaka zanu zimakhalabe pa mibado yonse. Onani mutuwo |