Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 102:23 - Buku Lopatulika

23 Iye analanda mphamvu yanga panjira; anachepsa masiku anga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Iye analanda mphamvu yanga panjira; anachepsa masiku anga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Chauta wathyola mphamvu zanga ndisanakule, wafupikitsa masiku anga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Iye anathyola mphamvu zanga pa nthawi ya moyo wanga; Iyeyo anafupikitsa masiku anga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 102:23
10 Mawu Ofanana  

Pakuti chomsamalitsa nyumba yake nchiyani, atapita iye, chiwerengo cha miyezi yake chitadulidwa pakati?


Ndipo padzakhala masiku otsiriza, kuti phiri la nyumba ya Yehova lidzakhazikika pansonga ya mapiri, ndipo lidzakwezedwa pamwamba pa zitunda; mitundu yonse idzasonkhana kumeneko.


Ndipo anthu ambiri adzanka, nati, Tiyeni tikwere kunka kuphiri la Yehova, kunyumba ya Mulungu wa Yakobo; ndipo Iye adzatiphunzitsa za njira zake, ndipo tidzayenda m'mayendedwe ake; chifukwa mu Ziyoni mudzatuluka chilamulo, ndi mau a Yehova kuchokera mu Yerusalemu.


Pa nthawi yomweyo adzatcha Yerusalemu mpando wa Yehova; ndipo mitundu yonse idzasonkhanidwa kumeneko, ku dzina la Yehova, ku Yerusalemu; ndipo sadzayendanso konse m'kuumirira kwa mtima wao woipa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa