Masalimo 102:22 - Buku Lopatulika22 Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu, ndi maufumu kuti atumikire Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Posonkhana pamodzi mitundu ya anthu, ndi maufumu kuti atumikire Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 pamene mitundu ya anthu ndi mafumu adzasonkhana kuti apembedze Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 pamene mitundu ya anthu ndi maufumu adzasonkhana kuti alambire Yehova. Onani mutuwo |