Masalimo 102:20 - Buku Lopatulika20 kuti amve kubuula kwa wandende; namasule ana a imfa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 kuti amve kubuula kwa wandende; namasule ana a imfa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 kuti amve kubuula kwa anthu am'ndende, kuti aŵapulumutse amene adaayenera kuphedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 kuti amve kubuwula kwa anthu a mʼndende, kuti apulumutse amene anayenera kuphedwa.” Onani mutuwo |