Masalimo 102:15 - Buku Lopatulika15 Pamenepo amitundu adzaopa dzina la Yehova, ndi mafumu onse a dziko lapansi ulemerero wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Pamenepo amitundu adzaopa dzina la Yehova, ndi mafumu onse a dziko lapansi ulemerero wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mitundu ya anthu idzalemekeza Chauta moopa, mafumu onse a pa dziko lapansi adzaopa ulemerero wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mitundu ya anthu idzaopa dzina la Yehova, mafumu onse a dziko lapansi adzalemekeza ulemerero wanu. Onani mutuwo |