Masalimo 102:14 - Buku Lopatulika14 Pakuti atumiki anu akondwera nayo miyala yake, nachitira chifundo fumbi lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pakuti atumiki anu akondwera nayo miyala yake, nachitira chifundo fumbi lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Mzindawo amaukondabetu anthu anu, ngakhale waonongeka ndi kusanduka bwinja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pakuti miyala yake ndi yokondedwa kwa atumiki anu; fumbi lake lokha limawachititsa kuti amve chisoni. Onani mutuwo |