Masalimo 102:13 - Buku Lopatulika13 Inu mudzauka, ndi kuchitira nsoni Ziyoni; popeza yafika nyengo yakumchitira chifundo, nyengo yoikika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Inu mudzauka, ndi kuchitira nsoni Ziyoni; popeza yafika nyengo yakumchitira chifundo, nyengo yoikika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mudzadzuka nkuchitira chifundo mzinda wa Ziyoni, zoonadi, nthaŵi yake youkomera mtima yafika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Inu mudzadzuka ndi kuchitira chifundo Ziyoni pakuti ndi nthawi yoti muonetse kukoma mtima kwanu pa iyeyo; nthawi yoyikika yafika. Onani mutuwo |