Masalimo 101:5 - Buku Lopatulika5 Wakuneneza mnzake m'tseri ndidzamdula; wa maso odzikuza ndi mtima wodzitama sindidzamlola. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wakuneneza mnzake m'tseri ndidzamdula; wa maso odzikuza ndi mtima wodzitama sindidzamlola. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Munthu wosinjirira mnzake kuseri ndidzamcheteketsa. Wooneka wonyada ndi wodzikuza sindidzamulekerera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aliyense wosinjirira mnansi wake mseri ameneyo ndidzamuletsa; aliyense amene ali ndi maso amwano ndi mtima wodzikuza, ameneyo sindidzamulekerera. Onani mutuwo |