Masalimo 101:4 - Buku Lopatulika4 Mtima wopulukira udzandichokera; sindidzadziwana naye woipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mtima wopulukira udzandichokera; sindidzadziwana naye woipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndidzakhala kutali ndi anthu a mtima woipa, sindidzalola choipa chilichonse kuloŵa mwa ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anthu a mtima wokhota adzakhala kutali ndi ine; ine sindidzalola choyipa chilichonse kulowa mwa ine. Onani mutuwo |