Masalimo 101:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzachita mwanzeru m'njira yangwiro; mudzandidzera liti? Ndidzayenda m'nyumba mwanu ndi mtima wangwiro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzachita mwanzeru m'njira yangwiro; mudzandidzera liti? Ndidzayenda m'nyumba mwanu ndi mtima wangwiro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzatsata njira yopanda cholakwa. Nanga mudzabwera liti kwa ine? Ndidzakhala ndi mtima wangwiro m'nyumba mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndidzatsata njira yolungama; nanga mudzabwera liti kwa ine? Ndidzayenda mʼnyumba mwanga ndi mtima wosalakwa. Onani mutuwo |