Masalimo 101:1 - Buku Lopatulika1 Ndidzaimba zachifundo ndi chiweruzo; ndidzaimba zakukulemekezani Inu, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndidzaimba zachifundo ndi chiweruzo; ndidzaimba zakukulemekezani Inu, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndidzaimba nyimbo zotamanda kukhulupirika ndi kulungama. Ndidzakuimbirani Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndidzayimba za chikondi ndi chiweruzo chanu cholungama; kwa Inu Yehova ndidzayimba matamando. Onani mutuwo |