Malaki 4:4 - Buku Lopatulika4 Kumbukirani chilamulo cha Mose mtumiki wanga, ndinamlamuliracho mu Horebu chikhale cha Israele yense, ndicho malemba ndi maweruzo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kumbukirani chilamulo cha Mose mtumiki wanga, ndinamlamuliracho m'Horebu chikhale cha Israele lonse, ndicho malemba ndi maweruzo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 “Kumbukirani zophunzitsa za Mose mtumiki wanga, malamulo ndi malangizo amene ndidamulamula ku phiri la Horebu kuti auze Aisraele onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse. Onani mutuwo |