Malaki 4:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo mudzapondereza oipa; pakuti adzakhala ngati mapulusa kumapazi anu, tsiku ndidzaikalo, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo mudzapondereza oipa; pakuti adzakhala ngati mapulusa kumapazi anu, tsiku ndidzaikalo, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsiku limene ndilikukonzalo mudzapondereza anthu oipa ngati phulusa ku mapazi anu. Ndikutero Ine Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. Onani mutuwo |