Luka 7:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo pamene iye anamva za Yesu, anatuma kwa Iye akulu a Ayuda, namfunsa Iye kuti adze kupulumutsa kapolo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo pamene iye anamva za Yesu, anatuma kwa Iye akulu a Ayuda, namfunsa Iye kuti adze kupulumutsa kapolo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mkuluyo atamva za Yesu, adatuma akulu ena a Ayuda kwa Iye kukampempha kuti adzachiritse wantchito wakeyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kenturiyo anamva za Yesu ndipo anatumiza ena a akulu Ayuda kwa Iye kuti abwere adzachiritse wantchito wakeyo. Onani mutuwo |