Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 7:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Kenturiyo anamva za Yesu ndipo anatumiza ena a akulu Ayuda kwa Iye kuti abwere adzachiritse wantchito wakeyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 Ndipo pamene iye anamva za Yesu, anatuma kwa Iye akulu a Ayuda, namfunsa Iye kuti adze kupulumutsa kapolo wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo pamene iye anamva za Yesu, anatuma kwa Iye akulu a Ayuda, namfunsa Iye kuti adze kupulumutsa kapolo wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mkuluyo atamva za Yesu, adatuma akulu ena a Ayuda kwa Iye kukampempha kuti adzachiritse wantchito wakeyo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:3
7 Mawu Ofanana  

Yesu atalowa mʼKaperenamu, Kenturiyo anabwera kwa Iye napempha chithandizo,


Kumeneko wantchito wa Kenturiyo, amene amamukhulupirira kwambiri, anadwala ndipo anali pafupi kufa.


Iwo atafika kwa Yesu, anamudandaulira kwambiri, nati, “Munthuyu ayenera kuthandizidwa


Nthawi yomweyo munthu wotchedwa Yairo, woweruza wa mu sunagoge, anabwera ndi kugwa pa mapazi a Yesu, namupempha Iye kuti apite ku nyumba kwake,


Munthu wina mʼgulu la anthulo anayitana kuti, “Aphunzitsi, ndikupemphani kuti muone mwana wangayu, pakuti ndi mmodzi yekhayu.


Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.


ndikukupempha chifukwa cha mwana wanga Onesimo, amene ndamubala ndili mu unyolo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa