Genesis 7:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu ndi limodzi, pamene chigumula cha madzi chinali padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Nowa anali wa zaka mazana asanu ndi limodzi, pamene chigumula cha madzi chinali pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Nowa anali wa zaka 600 pamene chigumulacho chidafika pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene chigumula chinabwera pa dziko lapansi Nowa anali ndi zaka 600. Onani mutuwo |