Genesis 11:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo dziko lapansi linali la chinenedwe chimodzi ndi chilankhulidwe chimodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Poyambayamba anthu onse a pa dziko lapansi ankalankhula chilankhulo chimodzi, ndipo mau amene ankalankhulawo anali amodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nthawi imeneyo anthu onse a pa dziko lapansi ankayankhula chiyankhulo chimodzi ndipo mawu amene ankayankhula anali amodzi. Onani mutuwo |