Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Filemoni 1:18 - Buku Lopatulika

18 Koma ngati anakulakwira kanthu, kapena wokongola kanthu, kanthu, kapena wakongola kanthu, undiwerengere ine kameneko;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Koma ngati anakulakwira kanthu, kapena wokongola kanthu, kanthu, kapena wakongola kanthu, undiwerengere ine kameneko;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Ngati adakulakwirapo, kapena ali ndi ngongole kwa iwe, ngongoleyo ikhale yanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ngati anakulakwira kapena kukongola kanthu kalikonse, ndidzalipira ineyo.

Onani mutuwo Koperani




Filemoni 1:18
4 Mawu Ofanana  

Ine ndidzakhala chikole, pa manja anga mudzamfunsa: ndikapanda kumbwezera kwa inu ndi kumuimitsa pamaso panu, chifukwa chake chidzakhala pa ine masiku onse:


Ngati tsono undiyesa woyanjana nawe, umlandire iye monga ine mwini.


ine Paulo ndichilemba ndi dzanja langa, ndidzachibwezera ine; kuti ndisanene nawe kuti iwe ndiwe mangawa anga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa