Filemoni 1:17 - Buku Lopatulika17 Ngati tsono undiyesa woyanjana nawe, umlandire iye monga ine mwini. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ngati tsono undiyesa woyanjana nawe, umlandire iye monga ine mwini. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono ngati umati ndine bwenzi lako, umlandire iyeyu monga momwe ukadandilandirira ineyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Tsono ngati umati ndine mnzako, umulandire iyeyu monga momwe ukanandilandirira ineyo. Onani mutuwo |