Eksodo 6:27 - Buku Lopatulika27 Awa ndi omwewo ananena ndi Farao, mfumu ya Aejipito, awatulutse ana a Israele mu Ejipito; Mose ndi Aroni amenewa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Awa ndi omwewo ananena ndi Farao, mfumu ya Aejipito, awatulutse ana a Israele m'Ejipito; Mose ndi Aroni amenewa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ameneŵa ndiwo ankauza Farao mfumu ya ku Ejipito kuti atulutse Aisraele ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Mose ndi Aaroni ndiwo amene anayankhula ndi Farao mfumu ya Igupto kuti atulutse Aisraeli mu Igupto. Onani mutuwo |