Eksodo 6:26 - Buku Lopatulika26 Omwewo ndiwo Aroni ndi Mose amene Yehova ananena nao, Tulutsani ana a Israele m'dziko la Ejipito mwa makamu ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Omwewo ndiwo Aroni ndi Mose amene Yehova ananena nao, Tulutsani ana a Israele m'dziko la Ejipito mwa makamu ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Mose ndi Aroni ndi omwe aja amene Chauta adaŵauza kuti, “Atulutseni Aisraele m'dziko la Ejipito mwa magulumagulu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Aaroni ndi Mose ndi aja amene Yehova anawawuza kuti, “Tulutsani Aisraeli mu Igupto mʼmagulu awo.” Onani mutuwo |