Eksodo 6:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yehova ananena kwa Mose, Tsopano udzaona chomwe ndidzachitira Farao; pakuti ndi dzanja lamphamvu adzawalola apite, inde ndi dzanja lamphamvu adzawaingitsa m'dziko lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehova ananena kwa Mose, Tsopano udzaona chomwe ndidzachitira Farao; pakuti ndi dzanja lamphamvu adzawalola apite, inde ndi dzanja lamphamvu adzawaingitsa m'dziko lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta adauza Moseyo kuti, “Uwona tsopano zimene ndimchite Farao. Ndidzakakamiza Farao kuti atulutse anthu anga m'dziko lake. Ndithudi, adzaŵatulutsiratu m'dzikomo, chifukwa ndidzamkakamiza ndi dzanja langa lamphamvu. Zoonadi, dzanja langa lamphamvu lidzamuumiriza kuti aŵapirikitse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anawuza Mose kuti, “Tsopano udzaona zimene ndimuchite Farao: Chifukwa cha dzanja langa lamphamvu adzalola anthu anga kuti atuluke. Chifukwa cha dzanja langa lamphamvu adzawatulutsa mʼdziko lake.” Onani mutuwo |