Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 40:4 - Buku Lopatulika

4 Ulongenso gomelo, nukonzerepo zokonzera zake; ulongenso choikaponyalicho, ndi kuyatsa nyali zake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ulongenso gomelo, nukonzerepo zokonzera zake; ulongenso choikapo nyalicho, ndi kuyatsa nyali zake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ukhazikemonso tebulo, pamwamba pake uikepo zipangizo zake, ndipo uikemo choikaponyale ndi nyale zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ulowetsemo tebulo ndi kuyika zimene zimakhala pamenepo. Kenaka ulowetse choyikapo nyale ndipo uyikepo nyale zake.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 40:4
7 Mawu Ofanana  

Ndipo uuze ana a Israele akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti awalitse nyali kosalekeza.


Nthawi zonse tsiku la Sabata aukonze pamaso pa Yehova, chifukwa cha ana a Israele, ndilo pangano losatha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa