Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 4:4 - Buku Lopatulika

4 Koma Yehova anati kwa Mose, Tambasula dzanja lako, nuigwire kumchira; ndipo anatambasula dzanja lake, naigwira, nikhalanso ndodo m'dzanja lake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma Yehova anati kwa Mose, Tambasula dzanja lako, nuigwire kumchira; ndipo anatambasula dzanja lake, naigwira, nikhalanso ndodo m'dzanja lake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Apo Chauta adauza Mose uja kuti, “Igwire mchira.” Mose adaigwira, pompo idasandukanso ndodo m'manja mwakemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Kenaka Yehova anati kwa iye, “Igwire mtchira.” Ndipo Mose anayigwira mchira njokayo ndipo inasandukanso ndodo mʼdzanja lake.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 4:4
9 Mawu Ofanana  

Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.


Udzaponda mkango ndi mphiri; udzapondereza msona wa mkango ndi chinjoka.


Ndipo ananena Iye, Iponye pansi. Naiponya pansi, ndipo inasanduka njoka; ndipo Mose anaithawa.


kuti akhulupirire kuti wakuonekera Yehova Mulungu wa makolo ao, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo.


adzatola njoka, ndipo ngakhale akamwa kanthu kakufa nako, sikadzawapweteka; adzaika manja ao pa odwala, ndipo adzachira.


Taonani, ndakupatsani ulamuliro wakuponda pa njoka ndi zinkhanira, ndi pa mphamvu iliyonse ya mdaniyo; ndipo kulibe kanthu kadzakuipsani konse.


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa