Eksodo 4:5 - Buku Lopatulika5 kuti akhulupirire kuti wakuonekera Yehova Mulungu wa makolo ao, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 kuti akhulupirire kuti wakuonekera Yehova Mulungu wa makolo ao, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, ndi Mulungu wa Yakobo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta adamuuza kuti, “Ukachite zimenezi, ndipo adzakhulupirira kuti Chauta, Mulungu wa makolo ao, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isaki, Mulungu wa Yakobe, adakuwonekeradi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova anati, “Ukachite zimenezi ndipo akakukhulupirira kuti Yehova, Mulungu wa makolo awo, Mulungu wa Abrahamu, Mulungu wa Isake ndi Mulungu wa Yakobo, wakuonekera iwe.” Onani mutuwo |