Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 4:30 - Buku Lopatulika

30 ndipo Aroni anawafotokozera mau onse amene Yehova adauza Mose, nachita zizindikiro zija pamaso pa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 ndipo Aroni anawafotokozera mau onse amene Yehova adauza Mose, nachita zizindikiro zija pamaso pa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Aroni adafotokozera atsogoleriwo zonse zimene Chauta adaauza Mose, ndipo adachita zozizwitsa zonse zija anthuwo akupenya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Ndipo Aaroni anawafotokozera zonse zimene Yehova ananena kwa Mose. Anachita zizindikirozo pamaso pa anthu onse,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 4:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anadza, naitana akulu a anthu, nawaikira pamaso pao mau awa onse amene Yehova adamuuza.


Ndipo Mose anayankha nati, Koma taonani, sadzakhulupirira ine, kapena kumvera mau anga; pakuti adzanena, Yehova sanakuonekere iwe.


Ndipo ukalankhule naye, ndi kumpangira mau; ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi m'kamwa mwake, ndipo ndidzakuphunzitsani inu chimene mukachite.


Ndipo iye adzakulankhulira iwe kwa anthu; ndipo kudzatero, kuti iye adzakhala kwa iwe ngati m'kamwa, ndi iwe udzakhala kwa iye ngati Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa