Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 4:26 - Buku Lopatulika

26 Pamenepo anati mkaziyo, Mkwati wamwazi iwe, chifukwa cha mdulidwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Pamenepo anati mkaziyo, Mkwati wamwazi iwe, chifukwa cha mdulidwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Choncho Chauta adamleka Mose osamupha. Ndiye pamene Zipora adanena kuti, “Ndiwe mkwati woomboledwa ndi magazi,” chifukwa cha kuumbalako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Choncho Yehova anamuleka Mose wosamupha. Pa nthawiyo, Zipora anati, “Mkwati wa magazi,” ponena za mdulidwe.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 4:26
2 Mawu Ofanana  

Koma Zipora anatenga mpeni wamwala, nadula khungu la mwana wake, naliponya pa mapazi ake; nati, Pakuti iwe ndiwe mkwati wanga wamwazi. Ndipo Iye anamleka.


Ndipo Yehova ananena ndi Aroni, Muka kuchipululu kukakomana ndi Mose. Ndipo anamuka, nakomana naye paphiri la Mulungu, nampsompsona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa