Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo anaika pomwepo mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo anaika pomwepo mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono adaikapo mizere inai ya miyala yokongola. Pa mzere woyamba adaika miyala ya rubi, topazi ndi garaneti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kenaka anayikapo mizere inayi ya miyala yokongola kwambiri. Mzere woyamba anayika miyala ya rubi, topazi ndi berili;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:10
6 Mawu Ofanana  

Topazi wa Kusi sufanana nayo, sailinganiza ndi golide wolongosoka.


Ndi miyalayi ikhale monga mwa maina a ana a Israele, khumi ndi awiri, monga maina ao; monga malochedwe a chosindikizira, yonse ikhale monga maina ao, kwa mafuko khumi ndi awiri.


Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.


Chinakhala chaphwamphwa; anachiomba chapachifuwa chopindika; utali wake dzanja limodzi, ndi kupingasa kwake dzanja limodzi, chinakhala chopindika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa