Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:11 - Buku Lopatulika

11 Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Pa mzere wachiŵiri adaika miyala ya emeradi, safiro ndi daimondi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 mzere wachiwiri anayikapo miyala ya emeradi, safiro ndi dayimondi;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uikepo miyala yoikikapo, mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba;


ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahaloni;


Ndipo anaika pomwepo mizere inai ya miyala; mzere wa odemu, pitida, ndi bareketi, ndiyo ya mzere woyamba.


Ndi mzere wachitatu wa lesemu, sibu, ndi akalama.


Unali mu Edeni, munda wa Mulungu, mwala uliwonse wa mtengo wake unali chofunda chako, sardiyo, topazi, diamondi, berulo, sohamu, ndi yaspi, safiro, nofeki, bareketi, ndi golide; malingaka ako ndi akazi ako anakutumikira tsiku lolengedwa iwe zinakonzekeratu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa