Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 39:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 mzere wachiwiri anayikapo miyala ya emeradi, safiro ndi dayimondi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

11 Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndi mzere wachiwiri wa nofeki, safiro, ndi yahalomu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Pa mzere wachiŵiri adaika miyala ya emeradi, safiro ndi daimondi.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:11
5 Mawu Ofanana  

Uyikepo mizere inayi ya miyala yokongola kwambiri. Mzere woyamba ukhale ndi miyala ya rubi, topazi ndi berili.


Mzere wachiwiri pakhale miyala ya emeradi, safiro ndi dayimondi;


Kenaka anayikapo mizere inayi ya miyala yokongola kwambiri. Mzere woyamba anayika miyala ya rubi, topazi ndi berili;


mzere wachitatu anayikapo miyala ya opera, agate ndi ametisiti;


Iwe unkakhala ngati mu Edeni, munda wa Mulungu. Miyala yokongola ya mitundu yonse: rubi, topazi ndi dayimondi, kirisoliti, onikisi, yasipa, safiro, kalineliyoni ndi berili ndiwo inali zofunda zako. Ndipo zoyikamo miyalayo zinali zagolide. Anakupangira zonsezi pa tsiku limene unalengedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa