Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 37:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo analiyengera mphete zinai zagolide pa miyendo yake inai; mphete ziwiri pa mbali yake imodzi, ndi mphete ziwiri pa mbali yake ina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo analiyengera mphete zinai zagolide pa miyendo yake inai; mphete ziwiri pa mbali yake imodzi, ndi mphete ziwiri pa mbali yake ina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Adapanga mphete zinai zagolide zonyamulira, nazimangirira ku ngodya zinai za bokosilo, uku ziŵiri uku ziŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iye anapanga mphete zinayi zagolide ndi kuzimangirira ku miyendo yake inayi ija, mbali ina ziwiri ndi mbali inanso ziwiri.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 37:3
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Alevi anasenza likasa la Mulungu pa mapewa ao, mphiko zili m'mwemo, monga Mose anawauza, monga mwa mau a Yehova.


Pakuti akerubi anafunyulula mapiko ao pamalo a likasa, ndi akerubi anaphimba likasa ndi mphiko zake pamwamba pake.


ndipo analikuta ndi golide woona m'kati ndi kunja, nalipangira mkombero wa golide pozungulira pake.


Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide.


Ndipo ndinati kwa iye, Mbuye wanga, mudziwa ndinu. Ndipo anati kwa ine, Iwo ndiwo akutuluka m'chisautso chachikulu; ndipo anatsuka zovala zao, naziyeretsa m'mwazi wa Mwanawankhosa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa