Eksodo 37:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anapanga mphete zinayi zagolide ndi kuzimangirira ku miyendo yake inayi ija, mbali ina ziwiri ndi mbali inanso ziwiri. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo analiyengera mphete zinai zagolide pa miyendo yake inai; mphete ziwiri pa mbali yake imodzi, ndi mphete ziwiri pa mbali yake ina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo analiyengera mphete zinai zagolide pa miyendo yake inai; mphete ziwiri pa mbali yake imodzi, ndi mphete ziwiri pa mbali yake ina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Adapanga mphete zinai zagolide zonyamulira, nazimangirira ku ngodya zinai za bokosilo, uku ziŵiri uku ziŵiri. Onani mutuwo |