Eksodo 3:10 - Buku Lopatulika10 Tiye tsopano, ndikutuma kwa Farao, kuti utulutse anthu anga, ana a Israele mu Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tiye tsopano, ndikutuma kwa Farao, kuti utulutse anthu anga, ana a Israele m'Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono iwe ndikukutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga Aisraele ku Ejipito.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kotero tsopano, pita. Ine ndikukutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga, Aisraeli mʼdziko la Igupto.” Onani mutuwo |