Eksodo 3:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kotero tsopano, pita. Ine ndikukutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga, Aisraeli mʼdziko la Igupto.” Onani mutuwoBuku Lopatulika10 Tiye tsopano, ndikutuma kwa Farao, kuti utulutse anthu anga, ana a Israele mu Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tiye tsopano, ndikutuma kwa Farao, kuti utulutse anthu anga, ana a Israele m'Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono iwe ndikukutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga Aisraele ku Ejipito.” Onani mutuwo |