Eksodo 3:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo tsopano, taona kulira kwa ana a Israele kwandifikira; ndapenyanso kupsinjika kumene Aejipito awapsinja nako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo tsopano, taona kulira kwa ana a Israele kwandifikira; ndapenyanso kupsinjika kumene Aejipito awapsinja nako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ine ndamva ndithu kulira kwa Aisraele, ndipo ndaŵaonadi mazunzowo amene Aejipito akuŵapsinja nawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ine ndamva ndithu kulira kwa Aisraeli, ndipo ndaona mmene Aigupto akuwazunzira. Onani mutuwo |