Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 27:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo apise mphiko m'mphetezo kuti mphikozo zikhale pa mbali ziwiri za guwa la nsembe polinyamula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo apise mphiko m'mphetezo kuti mphikozo zikhale pa mbali ziwiri za guwa la nsembe polinyamula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ponyamula guwalo, mphikozo azizipisa m'mphete za pa mbali ziŵiri za guwalo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pamene mukunyamula guwalo, muzilowetsa nsichizo mʼmphetemo mbali zonse ziwiri za guwalo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:7
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uzipanga mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi golide, kuti anyamulire nazo gome.


Ndipo upangire guwa la nsembe mphiko, mphiko za mtengo wakasiya, ndi kuzikuta ndi mkuwa.


Ndipo ulipangire mphete ziwiri zagolide pansi pa mkombero wake; uziike pa nthiti zake ziwiri, pa mbali zake ziwiri; zikhale zopisamo mphiko kulinyamula nazo.


Atatha Aroni ndi ana ake aamuna kuphimba malo opatulika, ndi zipangizo zake zonse za malo opatulika, pofuna kumuka am'chigono; atatero, ana a Kohati adze kuzinyamula; koma asakhudze zopatulikazo, kuti angafe. Zinthu izi ndizo akatundu a ana a Kohati m'chihema chokomanako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa