Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 27:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pamene mukunyamula guwalo, muzilowetsa nsichizo mʼmphetemo mbali zonse ziwiri za guwalo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

7 Ndipo apise mphiko m'mphetezo kuti mphikozo zikhale pa mbali ziwiri za guwa la nsembe polinyamula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo apise mphiko m'mphetezo kuti mphikozo zikhale pa mbali ziwiri za guwa la nsembe polinyamula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ponyamula guwalo, mphikozo azizipisa m'mphete za pa mbali ziŵiri za guwalo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:7
5 Mawu Ofanana  

Upange nsichi zamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide kuti azinyamulira tebulolo.


Upange nsichi zamtengo wa mkesha ndipo uzikutire ndi mkuwa.


Upange mphete ziwiri zagolide ndipo uzilumikize ku guwa mʼmunsi mwa mkombero, mphete ziwiri ku mbali zonse ziwiri zoyangʼanana. Mphetozo zizigwira nsichi zonyamulira guwalo.


“Aaroni ndi ana ake aamuna akamaliza kukutira ziwiya za ku malo wopatulika ndi zipangizo zopatulika zonse, ndipo akakonzeka kusamuka pamalopo, Akohati abwere kudzazinyamula koma asagwire zinthu zopatulikazo. Akatero adzafa. Izi ndizo zinthu zimene Akohati ayenera kunyamula mu tenti ya msonkhano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa