Eksodo 27:5 - Buku Lopatulika5 Nuwaike pansi pa khoma lamkati la guwa la nsembelo posungulira, kuti malukidwe alekeze pakati pa guwa la nsembelo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nuwaike pansi pa khoma lamkati la guwa la nsembelo posungulira, kuti malukidwe alekeze pakati pa guwa la nsembelo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Uike sefayo m'munsi mwake mwa chibumi cha guwalo, ndipo ilekeze pakati pa guwalo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Uyike sefayo mmunsi mwa khoma la guwa lansembelo, ndipo ilekezere pakati pa guwa lansembelo. Onani mutuwo |