Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 27:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Uyike sefayo mmunsi mwa khoma la guwa lansembelo, ndipo ilekezere pakati pa guwa lansembelo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Nuwaike pansi pa khoma lamkati la guwa la nsembelo posungulira, kuti malukidwe alekeze pakati pa guwa la nsembelo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Nuwaike pansi pa khoma lamkati la guwa la nsembelo posungulira, kuti malukidwe alekeze pakati pa guwa la nsembelo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Uike sefayo m'munsi mwake mwa chibumi cha guwalo, ndipo ilekeze pakati pa guwalo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 27:5
4 Mawu Ofanana  

Upange sefa yachitsulo chamkuwa ndipo mʼngodya zake zinayizo upangiremo mphete zamkuwa.


Upange nsichi zamtengo wa mkesha ndipo uzikutire ndi mkuwa.


Anapanga sefa yachitsulo chamkuwa ya guwa lansembelo kuti ikhale mmunsi mwa khoma la guwa lansembelo, kuchokera pansi mpaka pakati pa khoma la guwalo.


Kuchokera mʼngalande ya pansi padzakhala mpaka pa phaka lapansi mita imodzi, mulifupi mwake theka la mita. Kuchokera pa phaka lalingʼono mpaka pa phaka lalikulu, msinkhu wake ndi mamita awiri, mulifupi mwake ndi masentimita makumi asanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa