Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 23:5 - Buku Lopatulika

5 Ukaona bulu wa munthu wakudana nawe alikugona pansi ndi katundu wake, ndipo ukadaleka kuthandiza, koma uzimthandiza ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ukaona bulu wa munthu wakudana nawe alikugona pansi ndi katundu wake, ndipo ukadaleka kuthandiza, koma uzimthandiza ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Bulu wa mdani wako akagwa ndi katundu, usabzole ndi kumsiya, koma umthandize kuti adzuke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ngati uwona bulu wa munthu wina amene amakuda atagwa ndi katundu, usamusiye pomwepo, uwonetsetse kuti wamuthandiza.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 23:5
3 Mawu Ofanana  

Mdani wako akamva njala umdyetse, akamva ludzu ummwetse madzi.


Mukapenya ng'ombe kapena nkhosa ya mbale wako zilikusokera musamazilekerera, muzimbwezera mbale wanu ndithu.


Mukapenya bulu kapena ng'ombe ya mbale wanu, zitagwa m'njira, musamazilekerera; mumthandize ndithu kuziutsanso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa