Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 23:4 - Buku Lopatulika

4 Ukakomana ndi ng'ombe kapena bulu wa mdani wako zilinkusokera, uzimbwezera izo ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ukakomana ndi ng'ombe kapena bulu wa mdani wako zilimkusokera, uzimbwezera izo ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 “Ukaona ng'ombe ya mdani wako ikusokera, kapena bulu wake, utenge ukampatse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 “Ngati ukumana ndi ngʼombe kapena bulu wa mdani wako zitasochera, uwonetsetse kuti wazitenga kupita nazo kwa mwini wakeyo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 23:4
9 Mawu Ofanana  

Mdani wako akamva njala umdyetse, akamva ludzu ummwetse madzi.


kapena anapeza chinthu chotayika, nanenapo bodza, nalumbira pabodza; pa chimodzi cha izi zonse amachita munthu, ndi kuchimwapo;


koma Ine ndinena kwa inu, Kondanani nao adani anu, ndi kupempherera iwo akuzunza inu;


Penyani kuti wina asabwezere choipa womchitira choipa; komatu nthawi zonse mutsatire chokoma, kwa anzanu, ndi kwa onse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa