Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 2:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo anamuka munthu wa banja la Levi, natenga mwana wamkazi wa Levi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Munthu wina wa fuko la Levi adakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Ndipo munthu wina wa fuko la Levi anakwatira mkazi wa fuko lomwelo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 2:1
6 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene Israele anakhala m'dzikomo, Rubeni anamuka nagona ndi Biliha, mkazi wamng'ono wa atate wake: ndipo Israele anamva. Ana aamuna a Yakobo anali khumi ndi awiri:


Hadadi uja anathawa, iyeyo ndi a ku Edomu ena, akapolo a atate wake pamodzi naye, kunka ku Ejipito, Hadadiyo akali mwana.


Ndipo dzina lake la mkazi wake wa Amuramu ndiye Yokebede, mwana wamkazi wa Levi, wobadwira Levi mu Ejipito; ndipo iye anambalira Amuramu, Aroni ndi Mose, ndi Miriyamu mlongo wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa