Eksodo 2:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anaima mkaziyo, naona mwana wamwamuna; m'mene anamuona kuti ali wokoma, anam'bisa miyezi itatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anaima mkaziyo, naona mwana wamwamuna; m'mene anamuona kuti ali wokoma, anambisa miyezi itatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mkaziyo adatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna. Ataona kuti mwanayo ndi wokongola, adamubisa miyezi itatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mkaziyo anatenga pathupi ndipo anabereka mwana wamwamuna. Ataona kuti mwanayo anali wokongola, anamubisa kwa miyezi itatu. Onani mutuwo |