Eksodo 15:6 - Buku Lopatulika6 Dzanja lanu lamanja, Yehova, lalemekezedwa ndi mphamvu, dzanja lanu lamanja, Yehova, laphwanya mdani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Dzanja lanu lamanja, Yehova, lalemekezedwa ndi mphamvu, dzanja lanu lamanja, Yehova, laphwanya mdani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu Chauta dzanja lanu lamanja ndi laulemerero, chifukwa cha nyonga zake, dzanja lanu lamanja limatswanya adani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova, dzanja lanu lamanja ndi laulemerero chifukwa cha mphamvu zake. Ndithu Yehova, dzanja lanu lamanja linaphwanya mdani. Onani mutuwo |