Eksodo 15:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo ndi ukulu wanu waukulu mwapasula akuukira Inu; mwatumiza mkwiyo wanu, unawanyeketsa ngati chiputu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo ndi ukulu wanu waukulu mwapasula akuukira Inu; mwatumiza mkwiyo wanu, unawanyeketsa ngati chiputu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mumagonjetsa adani anu ndi ulemerero wanu wopambana. Ukali wanu woyaka ngati moto ukuŵatentha ngati mapesi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndi ulemerero wanu waukulu, munagonjetsa okutsutsani. Inu munatumiza mkwiyo wanu waukulu; ndipo unawapsereza ngati udzu. Onani mutuwo |