Eksodo 15:5 - Buku Lopatulika5 Nyanja inawamiza; anamira mozama ngati mwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Nyanja inawamiza; anamira mozama ngati mwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nyanja yozamayo idaŵaphimba onse, adamira mpaka pansi pa nyanja ngati miyala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Nyanja yakuya inawaphimba; Iwo anamira pansi ngati mwala.” Onani mutuwo |