Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 15:4 - Buku Lopatulika

4 Magaleta a Farao ndi nkhondo yake anawaponya m'nyanja; ndi akazembe ake osankhika anamira mu Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Magaleta a Farao ndi nkhondo yake anawaponya m'nyanja; ndi akazembe ake osankhika anamira m'Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 “Chauta adaponya m'nyanja magaleta a Farao pamodzi ndi gulu lake lankhondo, adammizira atsogoleri ake amphamvu m'Nyanja Yofiira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Magaleta a Farao ndi asilikali ake ankhondo Iye wawaponya mʼnyanja. Akatswiri ankhondo amphamvu a Farao amizidwa mʼNyanja Yofiira.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 15:4
5 Mawu Ofanana  

Inu ndinu woopsa; ndipo utauka mkwiyo wanu adzakhala chilili ndani pamaso panu?


Ndipo Miriyamu anawayankha, Imbirani Yehova, pakuti wapambanatu; kavalo ndi wokwera wake anawaponya m'nyanja.


ndi iwe ndidzathyolathyola kavalo ndi wokwera wake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa