Eksodo 12:5 - Buku Lopatulika5 Mwanawankhosa wanu azikhala wangwiro, wamwamuna, wa chaka chimodzi; muzimtenga ku nkhosa kapena ku mbuzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwanawankhosa wanu azikhala wangwiro, wamwamuna, wa chaka chimodzi; muzimtenga ku nkhosa kapena ku mbuzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mwanawankhosa wake adzakhale wopanda chilema, wamphongo, wa chaka chimodzi. Mungathe kusankhulanso mwanawambuzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ziweto zimene musankhe ziyenera kukhala zazimuna za chaka chimodzi, zopanda chilema, ndipo zikhale nkhosa kapena mbuzi. Onani mutuwo |