Eksodo 10:23 - Buku Lopatulika23 sanaonane, sanaukenso munthu pamalo pake, masiku atatu; koma kwa ana onse a Israele kudayera m'nyumba zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 sanaonane, sanaukenso munthu pamalo pake, masiku atatu; koma kwa ana onse a Israele kudayera m'nyumba zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Aejipitowo sankathanso kuwonana, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene adachoka pakhomo pake masiku atatu onsewo. Koma Aisraele okha ankakhala koŵala ndithu kuja ankakhalaku. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Palibe amene anatha kuona mnzake kapena kuchoka pa khomo pake kwa masiku atatu. Koma kumalo kumene kumakhala Aisraeli kunali kowala. Onani mutuwo |